Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 128
  • Zochitika za Padzikoli Zikusintha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika za Padzikoli Zikusintha
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Mawonekedwe a Dziko Lino Akusintha”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 128

Nyimbo 128

Zochitika za Padzikoli Zikusintha

Losindikizidwa

(1 Akorinto 7:31)

1. Mulungu anapereka

Mwana wake mmodzi yekha

Kuti zikhale zotheka

Kudzapulumutsidwa.

(KOLASI)

Ngakhale dzikoli

likusintha

Mulungu adzadalitsa

Dzikoli ndi kumwamba.

2. Dzikolitu likudwala

Kuvutika ndi kofala

Koma tikusangalala

Ufumu unabadwa.

(KOLASI)

Ngakhale dzikoli

likusintha

Mulungu adzadalitsa

Dzikoli ndi kumwamba.

(Onaninso Sal. 115:15, 16; Aroma 5:15-17; 7:25; Chiv. 12:5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena