Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 51
  • Timamatire Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Timamatire Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kumamatira kwa Yehova Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chipatso cha Kudziletsa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mulungu Wamkulu, Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani Okhazikika Monga Rute
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 51

Nyimbo 51

Timamatire Yehova

Losindikizidwa

(Yoswa 23:8)

1. Yehova ndi woyenera kulamulira.

Amachita zinthu zonse mwachilungamo.

Zonse zomwe wanena zimachitika.

Timumamatire, timuyandikire;

Ufumu wake ndi wopindulitsa.

2. Ulamuliro wake ndi wachilungamo.

Pokhala pakenso ndi paulemerero.

Iye aitana ofatsa abwere.

Timamatire M’lungu ndi wopambana;

Woyenera kuti tizimulambira.

3. M’mwamba ndi mosakwana kuti akhalemo.

Palibe wolepheretsa zofuna zake.

Adzakwaniritsa zomwe walonjeza.

Timumamatire, timutumikire,

Tikhale odziperekadi kwa iye.

(Onaninso Deut. 4:4; 30:20; 2 Maf. 18:6; Sal. 89:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena