Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 79
  • Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kukoma Mtima Ndi Kofunika Kwambiri
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukoma Mtima Ndi khalidwe Limene Limasonyezedwa M’mawu ndi Zochita
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • “Goli Langa Lili Lofeŵa, ndi Katundu Wanga Ali Wopepuka”
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Anthu a Mulungu Ayenera Kukonda Khalidwe la Kukoma Mtima
    Nsanja ya Olonda—2004
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 79

Nyimbo 79

Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Lofunika Kwambiri

Losindikizidwa

(Aefeso 4:32)

1. Tikuthokoza chifukwa choti

Yehova tam’dziwa.

Ngakhale n’ngwanzeru ndi wamphamvu,

Iye ndi wokoma mtima.

2. Yesu akuitana otopa

Awatsitsimule.

Ndipo goli lake ndi lofewa

Chifukwa n’ngokoma mtima.

3. Mulungu komanso Mbuye Yesu

Tiziwatsanzira.

M’zochita zathu tifunikira

Kukhala okoma mtima.

(Onaninso Mika 6:8; Mat. 11:28-30; Akol. 3:12; 1 Pet. 2:3.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena