LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
Baibo ya Cimasulilo ca Dziko Latsopano

Za m’Buku la 2 Akorinto

2 AKORINTO

ZA M’BUKULI

  • 1

    • Mau oyamba (1, 2)

    • Mulungu amatitonthoza pa masautso athu onse (3-11)

    • Paulo asintha mapulani a ulendo wake (12-24)

  • 2

    • Colinga ca Paulo cakuti Akorinto asangalale (1-4)

    • Wocimwa akhululukidwa ndipo abwezeletsedwa (5-11)

    • Paula afika ku Torowa ndi ku Makedoniya (12, 13)

    • Utumiki uli ngati kuguba pa cionetselo coonetsa kupambana (14-17)

      • Siticita nao malonda mau a Mulungu (17)

  • 3

    • Makalata ocitila umboni (1-3)

    • Atumiki a cipangano catsopano (4-6)

    • Ulemelelo wopambana wa cipangano catsopano (7-18)

  • 4

    • Kuwala kwa uthenga wabwino (1-6)

      • Maganizo a anthu osakhulupilila acititsidwa khungu (4)

    • Cuma m’ziwiya zadothi (7-18)

  • 5

    • Kubvala nyumba ya kumwamba (1-10)

    • Utumiki woyanjanitsa anthu ndi Mulungu (11-21)

      • Colengedwa catsopano (17)

      • Akazembe moimilako Khristu (20)

  • 6

    • Osagwilitsa nchito molakwa cisomo ca Mulungu (1, 2)

    • Paulo afotokoza utumiki wake (3-13)

    • Musamangidwe mu joko ndi wosakhulupilila (14-18)

  • 7

    • Tidziyeletse mwa kucotsa codetsa ciliconse (1)

    • Paulo ali ndi cimwemwe cifukwa ca Akorinto (2-4)

    • Tito abweletsa lipoti labwino (5-7)

    • Cisoni ca umulungu ndi kulapa (8-16)

  • 8

    • Zopeleka zopita kwa Akhristu a ku Yudeya (1-15)

    • Tito atumizidwa ku Korinto (16-24)

  • 9

    • Alimbikitsidwa kukhala opatsa (1-15)

      • Mulungu amakonda munthu amene amapeleka mocokela pansi pa mtima (7)

  • 10

    • Paulo akhalila kumbuyo utumiki wake (1-18)

      • Zida zathu za nkhondo si zam’dzikoli (4, 5)

  • 11

    • Paulo ndi atumwi apamwamba (1-15)

    • Mabvuto amene Paulo anakumana nao monga mtumwi (16-33)

  • 12

    • Masomphenya a Paulo (1-7a)

    • “Munga m’thupi” la Paulo (7b-10)

    • Paulo si wotsika pomuyelekezela ndi atumwi apamwamba (11-13)

    • Paulo adela nkhawa Akorinto (14-21)

  • 13

    • Macenjezo komanso malangizo omaliza a Paulo (1-14)

      • “Pitilizani kudziyesa kuti mutsimikize ngati mukali ndi cikhulupililo” (5)

      • Kusintha maganizo; kukhala amaganizo amodzi (11)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani