LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 9/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 9/15 masa. 1-2

Zamkati

September 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

OCTOBER 27, 2014–NOVEMBER 2, 2014

Kodi Mumakhulupilila Kuti Muli ndi Coonadi? N’cifukwa Ciani?

TSAMBA 7 • NYIMBO: 28, 107

NOVEMBER 3-9, 2014

Tumikilani Mulungu Mokhulupilika Panthawi ya “Masautso Ambili”

TSAMBA 12 • NYIMBO: 135, 133

NOVEMBER 10-16, 2014

Makolo—Wetani Ana Anu

TSAMBA 17 • NYIMBO: 88, 24

NOVEMBER 17-23, 2014

Imfa, Mdani Wotsilizila, Idzaonongedwa

TSAMBA 23 • NYIMBO: 111, 109

NOVEMBER 24-30, 2014

Muzikumbukila Amene Ali mu Utumiki Wanthawi Zonse

TSAMBA 28 • NYIMBO: 95, 100

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Kodi Mumakhulupilila Kuti Muli ndi Coonadi? N’cifukwa Ciani?

M’nkhani ino tidzaphunzila cifukwa cake anthu ambili amakhulupilila kuti Mboni za Yehova zili ndi coonadi. Tidzaphunzilanso cifukwa cake Mboni zimakhulupilila kuti zili ndi coonadi.

▪ Tumikilani Mulungu Mokhulupilika Panthawi ya “Masautso Ambili”

Timakumana ndi masautso cifukwa tikhala m’dziko la Satana. Mayeselo ena amabwela mwacindunji kuti afooketse cikhulupililo cathu ndipo ena mwakabisila. Nkhani ino idzatithandiza kuzindikila masautso amene Satana amabweletsa, ndi mmene tingakonzekelele.

▪ Makolo—Ŵetani Ana Anu

Makolo ali ndi udindo wolela ana ao “m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake.” (Aef. 6:4) M’nkhani ino, tidzakambilana zinthu zitatu zimene makolo angacite kuti akhale abusa a kuuzimu a ana ao.

▪ Imfa, Mdani Wotsilizila, Idzaonongedwa

Kodi imfa inaloŵa bwanji m’banja la anthu? Kodi ‘imfa, mdani wotsilizila, idzaonongedwa’ motani? (1 Akor. 15:26) Onani mmene mayankho akuunikila cilungamo ca Yehova, nzelu zake, ndi cikondi cake makamaka.

▪ Muzikumbukila Amene Ali mu Utumiki Wanthawi Zonse

Kuyambila nthawi yakale, Yehova wakhala ndi atumiki ake okhulupilika amene amam’tumikila mu utumiki wanthawi zonse, ngakhale kuti amakumana ndi mavuto m’dongosolo lino la zinthu. Tingacitenji kuti ‘tizikumbukila nchito zao zacikhulupililo, ndi nchito zao zacikondi’?—1 Ates. 1:3.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Kodi Mukukalamila Udindo?

22 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

CIKUTO: Abale aŵili alalikila uthenga wa m’Baibulo kwa msozi ku Negombo, kumadzulo kwa doko ku Sri Lanka

KU SRI LANKA

KULI ANTHU

20,860,000

OFALITSA

5,600

APAINIYA ANTHAWI ZONSE

641

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani