LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 135
  • Pirirani Mpaka pa Mapeto

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pirirani Mpaka pa Mapeto
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pilila Mpaka Mapeto
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tidzapilila Mosalekeza
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tidzapilila Mosalekeza
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalanibe Pafupi na Gulu la Yehova
    Gulu Lokhazikitsidwa Kucita Cifunilo ca Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 135

Nyimbo 135

Pirirani Mpaka pa Mapeto

(Mateyu 24:13)

1. Zomwe M’lungu walonjeza,

Zomwe taphunzira

Zimatithandiza kukhala

Anthu opirira.

Usaiwale kuti

Tsikulo layandikira.

Mayesero akabwera

Ukhalebe wolimba.

2. Chikondi chako kwa M’lungu

Chisazilaretu,

Upirirebe,

Ngakhale m’mayesero a’kulu.

Usakayikire

Kapenatu kuchita mantha,

Yehova ali pafupi

Adzakupulumutsa.

3. Amene adzapirire

Mpakana mapeto

Ndiye adzapulumuke

Ndi kudzapeza moyo.

Lola kuti kupirira

Kugwire ntchito yake.

Yehova adzachititsa

Kuti usangalale.

(Onaninso Aheb. 6:19; Yak. 1:4; 2 Pet. 3:12; Chiv. 2:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani