LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 12/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 12/15 masa. 1-2

Zamkati

December 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

FEBRUARY 2-8, 2015

‘Mvelani ndi Kumvetsa Tanthauzo Lake’

TSAMBA 6 • NYIMBO: 92, 120

FEBRUARY 9-15, 2015

Kodi ‘Mumamvetsa Tanthauzo la Malemba’?

TSAMBA 11 • NYIMBO: 97, 96

FEBRUARY 16-22, 2015

Tikhale Ogwilizana Pamene Mapeto a Dzikoli Ayandikila

TSAMBA 22 • NYIMBO: 107, 29

FEBRUARY 23, 2015–MARCH 1, 2015

Kodi Mumayamikila Zimene Munalandila?

TSAMBA 27 • NYIMBO: 89, 135

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ ‘Mvelani ndi Kumvetsa Tanthauzo Lake’

▪ Kodi ‘Mumamvetsa Tanthauzo la Malemba’?

Tingatsimikize bwanji kuti tikumvetsa zimene mafanizo a Yesu amatanthauza? Nkhani ziŵilizi zitithandiza kupenda mafanizo 7 amene Yesu anakamba. Zitithandizanso kudziŵa mmene tingagwilitsile nchito mfundo zimene tidzaphunzila m’mafanizo amenewa pa utumiki wathu wacikristu.

▪ Tikhale Ogwilizana Pamene Mapeto a Dzikoli Ayandikila

▪ Kodi Mumayamikila Zimene Munalandila?

M’dziko lino limene acinyamata ambili ndi odzikonda, n’cifukwa ciani Akristu acinyamata ayenela kugwilizana ndi anthu a Mulungu? M’nkhani izi tikambilana zitsanzo zabwino ndi zoipa ndiponso mfundo zimene zingathandize acinyamata ndi acikulile omwe kusankha zocita mwanzelu.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Njilayo ‘Anali Kuidziŵa’

4 Yehova Amadalitsa Kwambili Anthu Ofunitsitsa Kupeleka

16 Kodi Mukukumbukila?

17 Kodi Muyenela Kusintha Maganizo Anu?

21 Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi

32 Mlozela nkhani wa Nsanja ya Mlonda wa 2014

PA CIKUTO: Anthu amene amapita kukasangalala ku Tamarindo, malo amene ali m’mbali mwa nyanja ya Pacific m’dziko la Costa Rica, amasangalala akaphunzila kuti mtsogolomu dziko lonse lapansi lidzakhala paladaiso, ndipo mmenemo tizikalima ndi kusangalala

COSTA RICA

OFALITSA

29,185

APAINIYA

2,858

Dzina la Mulungu lakuti Yehova,

Jéoba

M’cinenelo ca Cibiribiri

Jehová

M’cinenelo ca Cikabeka

M’dzikoli muli mipingo iŵili ndi magulu aŵili amene amagwilitsila nchito cinenelo ca Cibiribiri, ndipo muli mipingo itatu ndi magulu anai amene amagwilitsila nchito cinenelo ca Cikabeka. Zonse ziŵili ndi zinenelo za anthu a ku America.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani