LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 October tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 October tsa. 2

Zamkati

3 Mbili Yanga​—Kucita Zimene Yehova Watilamula Kumabweletsa Madalitso

WIKI YA NOVEMBER 27, 2017–DECEMBER 3, 2017

7 “Tizisonyezana Cikondi Ceni-ceni m’Zocita Zathu”

Cikondi ceni-ceni cimadziŵikitsa Akhristu oona. Nkhani iyi idzafotokoza zinthu 9 zimene tingacite zoonetsa kuti tili na cikondi “copanda cinyengo.”—2 Akor. 6:6.

WIKI YA DECEMBER 4-10, 2017

12 Coonadi ‘Sicibweletsa Mtendele Koma Lupanga’

Ngati acibululu amatsutsa coonadi, umoyo wa mtumiki wa Yehova ungakhale wovuta. M’nkhani imeneyi, tidzaphunzila zimene tingacite kuti tipilile citsutso ca m’banja.

17 Yosefe wa ku Arimateya Analimba Mtima

WIKI YA DECEMBER 11-17, 2017

21 Mmene Masomphenya a Zekariya Amakukhudzilani

WIKI YA DECEMBER 18-24, 2017

26 Magaleta na Cisoti Cacifumu Zimakutetezani

Nkhani izi zidzafotokoza masomphenya a Zekariya a namba 6, 7, na 8. Masomphenya a namba 6 na 7 adzatithandiza kuyamikila mwayi wathu wotumikila m’gulu loyela la Mulungu. Masomphenya a namba 8, adzatithandiza kuona mmene Yehova amatetezela olambila ake kuti kulambila koona kupitilize.

31 Kuonetsa Kukoma Mtima Kamodzi Cabe

32 Kodi Mudziŵa?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani