LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 1/13 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 21

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 21
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JANUARY 21
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 1/13 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa January 21

MLUNGU WA JANUARY 21

Nyimbo 61 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 18 ndime 1-5, ndi mabokosi patsamba 142 ndi 144 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Mateyu 12-15 (Mph. 10)

Na. 1: Mateyu 14:23–15:11 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Ngati Wina Wanena Kuti, ‘Ngati Mukufuna Kundilalikila Uthenga Wanu, Mupemphele Kaye’—rs tsa. 342 ndime 7-8 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tikuphunzilapo Ciani pa Citsanzo ca Isaki Cokonda Kucita Zinthu Mwamtendele?—Gen. 26:19-22 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 32

Mph. 10: Lengezani Uthenga Wabwino Mwakhama. (Mac. 5:42) Kambilanani ndi wofalitsa mmodzi kapena aŵili acangu. Afunseni kuti afotokoze zimene zawathandiza kuona ulaliki kukhala wofunika. Kodi amacita ciani kuti akonzekele ulaliki? Nanga ulaliki wawathandiza bwanji kukhala olimba kuuzimu?

Mph. 10: Khalidwe Lathu Labwino Limapeleka Umboni. (1 Pet. 2:12) Kukambilana kozikidwa pa Nsanja ya Olonda ya April 15, 2012 tsa. 6-8, ndi Nsanja ya Olonda ya February 15, 2011 tsa. 29-30, ndime 13-16. Pemphani omvela kuti asimbe zimene aphunzilapo.

Mph. 10: “Kavalidwe Koyenela Kamalemekeza Mulungu.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 96 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani