LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 9/13 tsa. 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 23

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 23
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA SEPTEMBER 23
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 9/13 tsa. 7

Ndandanda ya Mlungu wa September 23

MLUNGU WA SEPTEMBER 23

Nyimbo 109 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jl phunzilo 3 mpaka 4 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: 2 Akorinto 8-13 (Mph. 10)

Na. 1: 2 Akorinto 10:1-18 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Ngati Wina Wanena Kuti, ‘Ndimakhulupilila Kuti Munthu Akafa Amakabadwanso Kwinakwake’—(rs tsa. 178 ndime 2-4) (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Lemba la 1 Akorinto 10:13 Limatanthauza Ciani? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 43

Mph. 5: “Ndidzatenga Mabuku Anu Mukatenga Anga.” Kukambitsilana. Pemphani omvela kuti afotokoze mmene agwilitsilila nchito malingalilo amenewa. Citani citsanzo cacidule.

Mph. 25: “Njila Zatsopano Zocitila Ulaliki Wapoyela.” Mafunso ndi mayankho. Fotokozani makonzedwe alionse amene mpingo wanu wapanga ocita ulaliki wapoyela mwa kugwilitsila nchito mathebulo kapena mashelufu a mawilo oikapo magazini ndi mabuku. Fotokozani kuti Mboni si ziyenela kutenga mabuku kapena magazini pa malo amenewa.

Nyimbo 44 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani