LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 2/14 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 3

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 3
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 3
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 2/14 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa March 3

MLUNGU WA MARCH 3

Nyimbo 112 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 5 ndime 7 mpaka 12 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Genesis 36-39 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 37:1-17 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Cifukwa Cimene Anthu Oukitsidwa Sadzalangidwila Nchito Zao Zakale—rs tsa. 111 ndime 4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Akristu Angaphunzile Ciani kwa Abigayeli?—1 Samueli 25:14-35 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 117

Mph. 10: Kugaŵila Magazini mu March. Nkhani yokambitsilana. Yambani mwa kucita citsanzo ca mmene mungagaŵilile magazini mwa kugwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo patsamba lino. Ndiyeno kambitsilanani ulaliki wonse kucokela kuciyambi mpaka kumapeto. Malizani mwa kupempha omvetsela kuti afotokoze mmene angagaŵilile magazini pamodzi ndi kapepala ka ciitano kumapeto kwa milungu iŵili yomaliza ya mwezi uno.

Mph. 10: Zosoŵa za pampingo.

Mph. 10: Kodi Tinacita Bwanji Mwezi Watha? Nkhani yokambitsilana. Pemphani ofalitsa kuti afotokoze mmene apindulila pogwilitsila nchito mfundo za m’nkhani yakuti, “Kuongolela Luso Lathu mu Ulaliki—Tizilemba Tikapeza Anthu Acidwi.” Pemphani omvela kuti afotokoze zocitika zosangalatsa za mu ulaliki.

Nyimbo 95 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani