LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 2/15 tsa. 3
  • Lengezani Coonadi Conena za Yesu Modzipeleka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Lengezani Coonadi Conena za Yesu Modzipeleka
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • M’Nyengo Ino ya Cikumbutso, Kodi Mudzatengela Kudzipeleka kwa Yehova ndi Yesu?
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 2/15 tsa. 3

Lengezani Coonadi Conena za Yesu Modzipeleka

Tikadziŵa njila zolengezela coonadi cokhudza Yesu timalalikila modzipeleka kwambili. Yesu ndi mwala wapakona womwe cikhulupililo coona cinamangidwapo. (Aef. 2:20) Popanda iye, tikanakhala tilibe ciyembekezo ca moyo wosatha. (Mac. 4:12) Conco, ndi pofunika kwambili kuti onse adziŵe malo amene Yesu ali nao pokwanilitsa colinga ca Mulungu. Anthu ambili asoceletsedwa ndi ziphunzitso zonama zimene si za m’malemba. Zomvetsa cisoni n’zakuti, sangalandile madalitso amene Mulungu walonjeza anthu amene ali ndi cikhulupililo mwa Yesu. Kudzipeleka pankhani ya coonadi kudzatisonkhezela kuthandiza anthu oona mtima kudziŵa bwino Yesu, ubale wake ndi Mulungu ndiponso udindo wake pokwanilitsa colinga ca Mulugu. Conco, m’nyengo ino ya Cikumbutso, kodi mudzalengeza coonadi conena za Yesu modzipeleka?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani