LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 6/15 tsa. 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 6

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 6
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JULY 6
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 6/15 tsa. 8

Ndandanda ya Mlungu wa July 6

MLUNGU WA JULY 6

Nyimbo 80 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 12 ndime 1-8 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Mafumu 7-8 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Mafumu 8:27-34 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Koneliyo—Mutu: Yehova Mulungu Alibe Tsankho—w14 9/15 tsa. 8 ndime 5-6 (Mph. 5)

Na. 3: Mungapilile Bwanji Nkhawa? —igw-CIN tsa. 24 ndime 1-3 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Kumbukilani masiku akale.”—Deut. 32:7.

Nyimbo 69

Mph. 10: Kugaŵila Magazini mu July. Kukambilana. Yambani ndi citsanzo coonetsa mmene mungagaŵile magazini pogwilitsila nchito maulaliki acitsanzo. Ndiyeno kambilanani maulaliki onse.

Mph. 10: Zosoŵa za pampingo.

Mph. 10: Tinacita Zotani? Kukambilana. Pemphani ofalitsa kuti afotokoze mmene apindulila pogwilitsila nchito mfundo za m’nkhani yakuti, “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuyambitsa Phunzilo la Baibulo Pogwilitsila Nchito Kabuku ka Uthenga Wabwino Wocokela Kwa Mulungu.” Pemphani omvela kuti afotokoze zocitika zosangalatsa za mu ulaliki.

Nyimbo 67 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani