LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 7/15 tsa. 4
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 7/15 tsa. 4

Maulaliki Acitsanzo

Nsanja ya Mlonda July-August

“Ngati munali ndi mphamvu yothetsa mavuto, kodi mukanathetsa vuto liti? [Yembekezani yankho.] Malinga ndi zimene Baibulo limafotokoza, Mulungu adzathetsa vuto limeneli ndi mavuto ena ambili. [Ŵelengani lemba logwilizana ndi vuto limene mwininyumba wakamba, monga Danieli 2:44; Miyambo 2:21, 22; Mateyu 7:21-23 ndi 2 Petulo 3:7.] Magazini iyi ifotokoza nthawi imene Mulungu adzabweletsa zinthu zosangalatsa ndi mmene adzacitila zimenezi.”

Galamukani! August

“Tikuonetsa anzathu nkhani yofotokoza kuculuka kwa zinthu zimene zili m’maselo a thupi lathu. [Muonetseni cikuto ca magazini a Galamukani!] Anthu ambili amakhulupilila kuti moyo unakhalako cifukwa ca cisanduliko, pamene ena amakhulupilila kuti unacita kulengedwa. Nanga inu muganiza bwanji? [Yembekezani ayankhe.] Magaziniyi ifotokoza zinthu zodabwitsa zimene zili m’maselo a thupi lathu, zimene zacititsa asayansi ena kuzindikila kuti moyo unapangidwa ndi Winawake.”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani