LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/15 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 26
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 26
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 10/15 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa October 26

MLUNGU WA OCTOBER 26

Nyimbo 15 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

ia mutu 1 ndime 1-13 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Mbiri 12-15 (Mph. 8)

Kubweleza za m’Sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: Khalani “ozikika mozama” ndi ‘okhazikika m’cikhulupililo.’—Akol. 2:6, 7.

Nyimbo 120

Mph. 10: Zogaŵila mu November. Kukambilana. Limbikitsani onse kugaŵila tumapepala twauthenga ndi buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa. Kambilanani mwacidule mfundo zothandiza za mu Utumiki Wathu wa Ufumu wa April 2014 pa mutu wakuti“ “Tumapepala Twauthenga Twatsopano Topangidwa Mosangalatsa.” Citani citsanzo ca ulaliki umene ungakhale wothandiza m’gawo lanu.

Mph. 20: “Kodi Mau a Mulungu Amagwila Nchito pa Umoyo Wanu?” Nkhani. Mukakamba mau oyamba acidule, lizani seŵelo la m’Baibulo la mau okha lopezeka pa jw.org kapena la pa CD lakuti “Musataye Mtima Pamene Yehova Akuongolelani!” Fotokozani mmene kusinkhasinkha Mau a Mulungu kungatithandizile kupeza mfundo zofunika kugwilitsila nchito paumoyo wathu. Malizani mwa kulimbikitsa onse kuti azimvetsela maseŵelo a m’Baibulo a mau okha opezeka pa jw.org.

Nyimbo 113 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani