LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/15 tsa. 3
  • Kodi Mau a Mulungu Amagwila Nchito pa Umoyo Wanu?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mau a Mulungu Amagwila Nchito pa Umoyo Wanu?
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • “Muzicita Zimene Mawu Amanena”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
  • Pitilizani Kusinkhasinkha Zinthu za Kuuzimu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Zimene Mungacite Kuti Muzipindula Kwambili Poŵelenga Baibo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 10/15 tsa. 3

Kodi Mau a Mulungu Amagwila Nchito pa Umoyo Wanu?

Kuŵelenga Baibulo tsiku ndi tsiku kungatithandize kukhala “ozikika mozama” ndi ‘okhazikika m’cikhulupililo.’ (Akol. 2:6, 7) Koma kuti Mau a Yehova azigwila nchito pa umoyo wathu, tifunika kuwasinkhasinkha ndi kucita zimene taphunzila. (Aheb. 4:12; Yak. 1:22-25) Lemba la Yoswa 1:8, limachula mbali zitatu zothandiza tikamaŵelenga Baibulo: (1) Kuŵelenga Mau a Mulungu “usana ndi usiku.” (2) “Kusinkhasinkha,” kutanthauza kuti tiyenela kuŵelenga paliwilo loyenela n’colinga cakuti tisinkhesinkhe ndi kuona zocitikazo m’maganizo mwathu. (3) Kutsimikiza mtima ‘kutsatila zonse zolembedwamo.’ Kucita zimenezi kudzatithandiza ‘kukhala ndi moyo wopambana.’ Kudzatithandizanso ‘kucita zinthu mwanzelu’ tsiku lililonse.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani