LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsa. 4
  • September 12-18

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • September 12-18
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 September tsa. 4

September 12-18

MASALIMO 120-134

  • Nyimbo 33 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (Mph. 3 kapena zocepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Thandizo Langa Licokela kwa Yehova”: (Mph. 10)

    • Sal. 121:1, 2—Popeza Yehova analenga zinthu zonse, tili ndi cifukwa comveka com’khulupilila (w04 12/15-CN, tsa. 12 ndime 3)

    • Sal. 121:3, 4—Yehova amakhala chelu nthawi zonse kuti aone zimene atumiki ake akufunikila (w04 12/15-CN, tsa. 12 ndime 4)

    • Sal. 121:5-8—Yehova ndi Mtetezi wokhulupilika wa anthu ake (w04 12/15-CN, tsa. 13 ndime 5-7)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (Mph. 8)

    • Sal. 123:2—Kodi fanizo la “maso a atumiki” lili na mfundo yabwanji? (w06 9/1-CN, tsa. 15 ndime 4)

    • Sal. 133:1-3—Ni phunzilo liti limene tingatengepo pa salimo imeneyi? (w06 9/1-CN, tsa. 16 ndime 3)

    • Kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno kwaniphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ni mfundo ziti pa kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ningaseŵenzetse mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibulo: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Sal.127:1–129:8

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 2 kapena zocepelapo) wp16. Na. 5 nkhani ya pacikuto—Kuyankha mwininyumba amene ni wokwiya.

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4 kapena zocepelapo) wp16. Na. 5 nkhani ya pacikuto—Itanilani mwininyumba kumisonkhano.

  • Phunzilo la Baibulo: (Mph. 6 kapena zocepelapo) fg phunzilo 8 ndime 6—Thandizani wophunzila kuti aziseŵenzetsa mfundo zimene waphunzila.

UMOYO WATHU WACIKHIRISTU

  • Nyimbo 114

  • Yehova Wanicitila Zambili: (Mph. 15) Tambitsani vidiyo ya pa jw.org. Yehova Wanicitila Zambili. (Pitani pa ZOKHUDZA IFE > ZIMENE TIMACITA.) Kambilanani mafunso otsatilawa: Kodi Yehova anam’thandiza bwanji Crystal? Nanga zimenezi zinam’limbikitsa bwanji? N’ciani cimene anali kucita akayamba kudziona kuti ni wosafunika? Kodi nkhani ya Crystal yakuthandizani bwanji?

  • Phunzilo la Baibulo la Mpingo: (Mph. 30) ia Mawu Omaliza ndime 1-13

  • Kubwelelamo ndi Kuchulako za Mlungu Wotsatila (Mph. 3)

  • Nyimbo 119 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani