LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsa. 2
  • “Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Atumiza Yeremiya Kuti Akalalikile
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yeremiya Sanaleke Kulankhula za Yehova
    Phunzitsani Ana Anu
  • Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Leka ‘Kufuna-funa Zinthu Zazikulu’
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 March tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 1-4

“Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”

Yopulinta

Yeremiya ayenela kuti anali na zaka pafupi-fupi 25 pamene Yehova anamuika kukhala mneneli. Yeremiya anadziona kuti ni wosayenelela udindowo, koma Yehova anam’tsimikizila kuti adzapitiliza kum’thandiza.

Mneneli Yeremiya aikidwa m’matangaza, apulumutsidwa m’citsime camatope, ndipo alila cifukwa ca kuwonongedwa kwa Yerusalemu
  1. 647

    Yeremiya aikidwa kukhala mneneli

  2. 607

    Yerusalemu awonongedwa

  3. 580

    Atsiliza kulemba

Madeti onse ni a mu B.C.E.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani