CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 1-4
“Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”
Yopulinta
Yeremiya ayenela kuti anali na zaka pafupi-fupi 25 pamene Yehova anamuika kukhala mneneli. Yeremiya anadziona kuti ni wosayenelela udindowo, koma Yehova anam’tsimikizila kuti adzapitiliza kum’thandiza.
647
Yeremiya aikidwa kukhala mneneli
607
Yerusalemu awonongedwa
580
Atsiliza kulemba
Madeti onse ni a mu B.C.E.