LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsa. 3
  • Analeka Kucita Cifunilo ca Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Analeka Kucita Cifunilo ca Mulungu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani Wolimba Mtima Monga Yeremiya
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yeremiya Sanaleke Kulankhula za Yehova
    Phunzitsani Ana Anu
  • Yehova Atumiza Yeremiya Kuti Akalalikile
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mwamuna Wosaopa Munthu
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 March tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 5-7

Analeka Kucita Cifunilo ca Mulungu

7:1-4, 8-10, 15

  • Molimba mtima, Yeremiya anavumbula macimo a Aisiraeli na cinyengo cawo

  • Aisiraeli anali kuona kacisi monga cithumwa cowateteza

  • Yehova anawaonetsa kuti nsembe zawo zamwambo sizinalungamitse macimo awo

Dzifunseni kuti: Ningacite ciani kuti kulambila kwanga kukhale kogwilizana na cifunilo ca Mulungu osati kwamwambo cabe?

Yeremiya akulengeza uthenga wa Yehova pacipata ca kacisi

Yeremiya ali pacipata ca nyumba ya Yehova

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani