LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 September tsa. 4
  • September 17-23

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • September 17-23
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 September tsa. 4

September 17-23

YOHANE 5-6

  • Nyimbo 2 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Tsatilani Yesu na Colinga Cabwino”: (10 min.)

    • Yoh. 6:9-11—Yesu mozizwitsa anadyetsa khamu la anthu (“amuna pafupi-fupi 5,000 anakhaladi pansi” nwtsty mfundo younikila pa Yoh. 6:10)

    • Yoh. 6:14, 24—Anthu atazindikila kuti Yesu anali Mesiya, tsiku lotsatila anayamba kumufuna-funa (“mneneli uja” mfundo younikila pa Yoh. 6:14)

    • Yoh. 6:25-27, 54, 60, 66-69—Popeza kuti anthuwo anali kutsatila Yesu na ophunzila ake pa zolinga zadyela, anakhumudwa na mawu ake (“cakudya cimene cimawonongeka. . . cakudya cokhalitsa, copeleka moyo wosatha”, “Wakudya mnofu wanga ndi kumwa magazi anga” nwtsty mfundo zounikila pa Yoh. 6:27, 54; w05 9/1 peji 21 mapa. 13-14)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yoh. 6:44—Kodi Atate amawakokela bwanji anthu kwa iyemwini? (“kukokedwa” nwtsty mfundo younikila)

    • Yoh. 6:64—Yesu anadziŵa “kucokela pa ciyambi” kutiYudasi ndiye adzamupeleka. Kodi n’kucokela pa ciyambi pati? (“Yesu anadziŵa . . . amene adzamupeleka,” “kucokela pa ciyambi” nwtsty mfundo zounikila)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Yoh. 6:41-59

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Mwininyumba akambe zimene anthu a m’gawo lanu amakonda kukamba pofuna kupewa kuwalalikila.

  • Kubwelelako Koyamba: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Mwininyumba akukuuzani kuti ni Mkhristu.

  • Vidiyo ya Kubwelelako Kaciŵili: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 31

  • Kodi Zinayenda Bwanji?: (5 min.) Kukambilana. Pemphani omvela kuti afotokoze mmene zinayendela atayesa kuyambitsa makambilano otsogolela ku ulaliki.

  • “Sipanawonongeke Ciliconse”: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Kamangidwe Kosawononga Cilengedwe Kamalemekezetsa Yehova—Kambali Kake.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu. 35 mapa. 28-36

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 89 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani