LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsa. 2
  • January 7-13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • January 7-13
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 January tsa. 2

January 7-13

MACHITIDWE 21-22

  • Nyimbo 55 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Cifunilo ca Yehova Cicitike”: (10 min.)

    • Mac. 21:8-12—Akhristu anzake anamucondelela Paulo kuti asapite ku Yerusalemu, cifukwa ca zoopsa zimene zinali kudzamucitikila (bt mape. 177-178 mapa. 15-16)

    • Mac. 21:13—Paulo anatsimikiza mtima kucita cifunilo ca Yehova (bt peji 178 pala. 17)

    • Mac. 21:14—Abalewo ataona kuti Paulo walimbikila kupita, anamuleka (bt peji 178 pala. 18)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Mac. 21:23, 24—Popeza kuti Akhristu sanali pansi pa Cilamulo ca Mose, n’cifukwa ciani akulu a ku Yerusalemu anapatsa Paulo malangizo aya? (bt mape. 184-185 mapa. 10-12)

    • Mac. 22:16—Kodi macimo a Paulo anasambitsidwa bwanji? (“kusamba kuti ucotse macimo ako mwa kuitana pa dzina lake” nwtsty mfundo younikila)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mac. 21:1-19 (th phunzilo 5)a

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Mawu Oyamba Ogwila Mtima, ndiyeno kambilanani phunzilo 1 m’kabulosha ka Kuphunzitsa.

  • Nkhani: (5 min. olo kucepelapo) w10 2/1 peji 13 pala. 2 mpaka peji 14 pala. 2—Mutu: Kodi Akhristu Ayenela Kusunga Sabata ya Wiki Iliyonse? (th phunzilo 1)b

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 134

  • “Yehova Anatiphunzitsa Kulela Bwino Ana Athu”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 49

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 70 na Pemphelo

a b Cidziŵitso: Kuyambila na Kabuku kano ka Msonkhano wa Umoyo na Utumiki, namba ya phunzilo ya wam’sukulu aliyense izikhala m’mabulaketi (). Malangizo amene wam’sukulu afunika kugwililapo nchito azicoka m’kabulosha kakuti Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa (th)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani