LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 February tsa. 5
  • Kodi Mukuyembekezela Mwacidwi?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mukuyembekezela Mwacidwi?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Yembekezelanibe!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Nyamula Mtengo Wako Wozunzikilapo ndi Kunditsatila Mosalekeza
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 February tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 7-8

Kodi Mukuyembekezela Mwacidwi?

8:19-21

  • “Cilengedwe”: anthu amene ali na ciyembekezo cokakhala padziko lapansi

  • ‘Kuonekela kwa ana a Mulungu’: nthawi pamene odzozedwa adzathandiza Khristu kuwononga dongosolo loipa la Satana

  • “Maziko a ciyembekezo”: lonjezo la Yehova lotipulumutsa kupitila mu imfa ya Yesu na kuukitsidwa kwake

  • ‘Kumasulidwa ku ukapolo wa kuvunda’: kumasulidwa pang’ono-pang’ono kucoka ku ucimo na imfa

M’bale wacicepele akucita phunzilo la umwini, akupeleka ndemanga pamisonkhano, akukana mtsikana amene akumufuna, ndiponso akucita zosangalatsa zoyenela

Mungaonetse bwanji kuti mukuyembekezela “mwacidwi nthawi imene ulemelelo wa ana a Mulungu udzaonekele”?

  • Muziŵelenga Baibo mwakhama na kupempha mzimu woyela

  • Muziseŵenzetsa mokwanila zinthu zauzimu zimene Yehova wakupatsani kuti mumuyandikile

  • Musalole Satana kukupangitsani kuganiza kuti njila za Mulungu n’zovuta kuzitsatila

  • Gwilitsitsani coonadi, na kucipanga kukhala canu-canu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani