LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsa. 8
  • Kodi Mudzacita Ciani pa Nthawi ya Cilala?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mudzacita Ciani pa Nthawi ya Cilala?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • N’zotheka Kuti Muziwadalila Abale Anu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • “Inu Mulungu Wanga, Cikhulupililo Canga Cili mwa Inu”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Kodi Mumakhulupilila Mmene Yehova Amacitila Zinthu?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • 10 Kudalilika
    Galamuka!—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 September tsa. 8
Mtengo wobyalidwa m’mbali mwa madzi umabeleka zipatso

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kodi Mudzacita Ciani pa Nthawi ya Cilala?

Cikhulupililo na cidalilo zimayendela limodzi. Mwacitsanzo, kukhulupilila kwambili Yehova kumatithandiza kukhala na cidalilo cakuti adzatiteteza na kutisamalila. (Sal. 23:1, 4; 78:22) Pamene mapeto a dongosolo lino la zinthu akutiyandikila, Satana adzatiukila koopsa. (Chiv. 12:12) N’ciani cidzatithandiza pa nthawiyo?

TAMBITSANI VIDIYO YAKUTI KODI MUDZACITA CIANI PA NTHAWI YA CILALA? PAMBUYO PAKE, KAMBILANANI MAFUNSO AYA:

  1. Kodi tingafanane bwanji na “mtengo” wochulidwa pa Yeremiya 17:8?

  2. Chulankoni vuto limodzi limene lili ngati “kutentha.”

  3. Kodi “mtengo” uja unakhudzidwa bwanji? Nanga n’cifukwa ciani?

  4. Kodi Satana amafuna kuwononga ciani?

  5. Kodi tili ngati anthu ojaila kuyenda pa ndeke m’njila yanji?

  6. N’cifukwa ciani tifunika kupitiliza kukhulupilila kapolo wokhulupilika ndi wanzelu? Nanga kodi kukhulupilika kwathu kungayesedwe bwanji?

  7. N’cifukwa ciani tifunika kupitiliza kukhulupilila mfundo za m’Baibo olo kuti ena atiseke?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani