LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsa. 4
  • Cifukwa Cake Cikhulupililo N’cofunika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cifukwa Cake Cikhulupililo N’cofunika
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Cikhulupililo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
  • Tengelani Cifundo ca Yesu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • “Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 September tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AHEBERI 11

Cifukwa Cake Cikhulupililo N’cofunika

11:1, 6, 33-38

Kodi kukhala na cikhulupililo colimba kungakuthandizeni bwanji m’zocitika zotsatilazi?

  • Woyang’anila dela mu Africa akulemba lipoti pa sanga pamene aima kuti agone ali mkati mwa ulendo wawo

    Mukauzidwa kucita utumiki umene muona kuti ni wovuta.—Aheb. 11:8-10

  • Banja lofeledwa lazungulila bokosi lokhala na maluŵa pamwamba pake

    Pamene mwatayikilidwa wokondedwa wanu mu imfa—Aheb. 11:17-19

  • Pa cisautso cacikulu, mabanja ocepa akhala pansi m’nyumba ndipo akuphunzila Baibo pamodzi m’nyumba

    Ngati boma lakulandani ufulu pankhani yolambila.—Aheb. 11:23-26

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani