LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsa. 5
  • Cilango—Umboni Wakuti Yehova Amatikonda

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cilango—Umboni Wakuti Yehova Amatikonda
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Cilango Cimaonetsa Cikondi ca Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Timaonetsa Cikondi Ngati Ticita Zinthu Mogwilizana na Cilango ca Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Cilango Ni Umboni Wakuti Mulungu Amatikonda
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Mmene Mungalangile Ana Anu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 September tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AHEBERI 12-13

Cilango—Umboni Wakuti Yehova Amatikonda

12:5-7, 11

Mayi akuŵelengela mwana wake wamkazi buku lakuti “Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso”

Cilango cimatanthauza kukwapula, kuwongolela, kulangiza, na kuphunzitsa. Monga mmene tate wacikondi amalangila ana ake, Yehova naye amatilanga. Timalandila cilango cake mwa njila izi . . .

  • Kuŵelenga Baibo, kucita phunzilo laumwini, kupezeka pa misonkhano, na kusinkha-sinkha

  • Wokhulupilila mnzathu akatipatsa uphungu kapena kutiwongolela

  • Zotulukapo za kulakwa kwathu

  • Kudzudzulidwa kapena kucotsedwa mu mpingo

  • Kukumana na mayeselo kapena cizunzo cimene Yehova walola.—w15 9/15 21 ¶13; it-1 629

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani