LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsa. 5
  • January 20-26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • January 20-26
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 January tsa. 5

January 20-26

GENESIS 6-8

  • Nyimbo 89 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Anacitadi Momwemo”: (10 min.)

    • Gen. 6:9, 13—Munthu wolungama Nowa anali kukhala pakati pa anthu oipa (w18.02 4 ¶4)

    • Gen. 6:14-16—Nowa anapatsidwa nchito yovuta (w13 4/1 14 ¶1)

    • Gen. 6:22—Nowa anali na cikhulupililo mwa Yehova (w11 9/15 18 ¶13)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Gen. 7:2—Kodi cosiyanitsila pakati pa nyama zodetsedwa na zosadetsedwa maka-maka cinali ciani? (w04 1/1 29 ¶7)

    • Gen. 7:11—Kodi madzi amene anacititsa Cigumula pa dziko lonse ayenela kuti anacokela kuti? (w04 1/1 30 ¶1)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni cuma ca kuuzimu citi cimene mwapeza ponena za Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mfundo ina?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 6:1-16 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi, ndiyeno funsani omvetsela mafunso otsatilawa: Kodi wofalitsa wathandiza bwanji mwininyumba kumvetsetsa mfundo ya pa 1 Yohane 4:8? Kodi ofalitsa athandizana bwanji polalikila?

  • Ulendo Wobwelelako Woyamba: (4 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 12)

  • Ulendo Wobwelelako Woyamba: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno gaŵilani cofalitsa ca mu Thuboksi Yathu. (th phunzilo 7)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 31

  • Kulambila Kwa Pabanja: Nowa—Anayenda na Mulungu: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi (pitani ku mavidiyo pa BANJA). Ndiyeno kambilanani mafunso aya: Kodi makolo m’vidiyoyi anaseŵenzetsa bwanji nkhani ya Nowa pophunzitsa ana awo mfundo zofunika? Ni zinthu ziti zothandiza zimene muona kuti mungaziseŵenzetse pocita kulambila kwanu kwa pabanja?

  • Zofunikila za Mpingo: (5 min.)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 100

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 37 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani