LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsa. 5
  • “Anacitadi Momwemo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Anacitadi Momwemo”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Anam’sunga “Pomupulumutsa Pamodzi ndi Anthu Ena 7”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Nowa Apanga Cingalawa
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Gao 5
    Mvetselani kwa Mulungu
  • Cingalawa ca Nowa
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 January tsa. 5
Nowa na ana ake akumanga cingalawa; mwana wake wakwela pa sikafodi ndipo akumata cingalawa na phula.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 6-8

“Anacitadi Momwemo”

6:9, 13-16, 22

Ganizilani kukula kwa nchito imene Nowa na banja lake anafunika kugwila pomanga cingalawa. Iwo analibe zipangizo zamakono kapena njila zatsopano zomangila.

  • Cingalawa cinali cacikulu—m’litali cinali mamita pafupi-fupi 133, m’lifupi mamita 22, msinkhu mamita 13

  • Anafunika kugwetsa mitengo, kuidula m’masaizi oyenela, ndiponso kuinyamula na kukaiika pa malo ake

  • Anafunika kumata phula cingalawa conse mkati na kunja komwe

  • Nowa na banja lake anafunika kusonkhanitsa cakudya cimene adzadya kwa caka, cawo komanso ca nyama

  • Nchitoyo iyenela kuti inatenga zaka 40 mpaka 50 kuti ithe

Kodi nkhaniyi ingatithandize bwanji ngati tiona kuti n’zovuta kucita zimene Yehova watipempha?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani