LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsa. 6
  • January 27–February 2

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • January 27–February 2
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 January tsa. 6

January 27–February 2

GENESIS 9-11

  • Nyimbo 101 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Padziko Lonse Lapansi Panali Cilankhulo Cimodzi”: (10 min.)

    • Gen. 11:1-4—Anthu ena anaganiza zomanga mzinda na nsanja yake motsutsana na cifunilo ca Mulungu (it-1 239; it-2 202 ¶2)

    • Gen. 11:6-8—Yehova anasokoneza citundu cawo (it-2 202 ¶3)

    • Gen. 11:9—Anthuwo analeka kumanga nsanjayo na mzinda wake, ndipo anabalalikana (it-2 472)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Gen. 9:20-22, 24, 25—N’cifukwa ciani Nowa anatembelela Kanani m’malo mwa Hamu? (it-1 1023 ¶4)

    • Gen. 10:9, 10—Kodi Nimurodi anali “mlenje wamphamvu wotsutsana na Yehova” m’njila yotani? (it-2 503)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni cuma ca kuuzimu citi cimene mwapeza ponena za Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mfundo ina?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 10:6-32 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Waciŵili: (5 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi, ndiyeno funsani omvetsela mafunso otsatilawa: N’ciani caonetsa kuti ofalitsawa anakonzekela pamodzi ulendo wobwelelako umenewu? Kodi m’baleyu wagaŵila motani cofalitsa ca mu Thuboksi Yathu na kuyambitsa phunzilo la Baibo?

  • Ulendo Wobwelelako Waciŵili: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 4)

  • Phunzilo la Baibo: (5 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo a ulendo wobwelelako waciŵili, ndiyeno yambitsani phunzilo la Baibo mwa kuseŵenzetsa buku lakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse. (th phunzilo 2)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 60

  • “Khalani Mmisili Waluso”: (15 min.) Nkhani yokambilana, yokambiwa na woyang’anila nchito.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 101

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 56 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani