LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 January tsa. 10
  • Zimene Tingacite Kuti Tilandile Madalitso a Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Tingacite Kuti Tilandile Madalitso a Yehova
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Amapatula Anthu Ake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • N’cifukwa Ciyani Tiyenela Kukhala Okhutila Komanso Odzicepetsa?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Zikondwelelo Zapacaka Zokhala na Tanthauzo kwa Ife
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Caka ca Ufulu Komanso Ufulu Wam’tsogolo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 January tsa. 10

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zimene Tingacite Kuti Tilandile Madalitso a Yehova

Pewani kulambila milungu yopanda pake (Lev. 26:1; w08 4/15 4 ¶8)

Lambilani Yehova mmene iye amafunila (Lev. 26:2; it-1 223 ¶3)

Muzimvela malamulo ake (Lev. 26:3, 12; w91 3/1 17 ¶10)

Aisiraeli amene anali kuyesetsa kutsatila malamulo a Yehova anali kukhala pa ubwenzi wabwino na iye, komanso anali kulandila madalitso ambili.

Banja lacimwemwe likucita ulaliki wapoyela pamene anthu odutsa akugula zinthu na kuyendetsa magalimoto odula.

Pa zinthu zotsatilazi, ni ziti zimene imwe muli nazo kaamba ka dalitso la Yehova?

  • Cidziŵitso colondola ca m’Baibo

  • Mtendele wa maganizo

  • Banja lacimwemwe

  • Ciyembekezo ca tsogolo labwino

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani