LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 34
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikhala Monga mwa Dzina Lathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nchito Yoonetsa Cikondi Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
  • ‘Talaŵani, Muone Kuti Yehova ni Wabwino’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 34

Nyimbo 34

Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu

(Yesaya 43:10-12)

1. Yehova wamphamvu yonse wam’yaya,

Wangwiro m’chilungamo, m’chikondi.

Ndinu gwero la cho’nadi ndi nzeru,

Mulamula monga Mfumu m’mwamba.

Timakondwa pokutumikirani

Ndiponso kulengeza Ufumu.

(KOLASI)

Ndi mwayidi kukhala Mboni zanu,

Tichite monga mwa dzina lathu.

2. Pokutumikirani ndi abale

Timakhaladi mogwirizana.

Pophunzitsa ena cho’nadi chanu,

Timakhalanso osangalala.

Timadziwikanso ndi dzina lanu,

Ndi mwayi wathu kulitchukitsa.

(KOLASI)

Ndi mwayidi kukhala Mboni zanu,

Tichite monga mwa dzina lathu.

(Onaninso Deut. 32:4; Sal. 43:3; Dan. 2:20, 21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani