LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 29
  • Tikhala Monga mwa Dzina Lathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikhala Monga mwa Dzina Lathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • Nchito Yoonetsa Cikondi Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
  • ‘Talaŵani, Muone Kuti Yehova ni Wabwino’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 29

NYIMBO 29

Tikhala Monga mwa Dzina Lathu

Yopulinta

(Yesaya 43:10-12)

  1. 1. Yehova M’lungu ndinu wamuyaya,

    Nchito zanu zonse ni zangwilo.

    Ndinu gwelo la co’nadi na nzelu,

    Inu mulamulila kumwamba.

    Timakondwa kukutumikilani,

    Kulengeza za Ufumu wanu.

    (KOLASI)

    Tinyadila kukhala Mboni zanu,

    Tikhala monga mwa dzina lathu!

  2. 2. Ni mwayi wathu kukuchukitsani

    Pophunzitsa ena coonadi.

    Utumiki umene mwatipatsa,

    Umatibweletsela cimwemwe.

    Lomba tidziŵika na dzina lanu,

    Ticitile umboni za inu.

    (KOLASI)

    Tinyadila kukhala Mboni zanu,

    Tikhala monga mwa dzina lathu!

(Onaninso Deut. 32:4; Sal. 43:3; Dan. 2:20, 21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani