LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 91
  • Nchito Yoonetsa Cikondi Cathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Nchito Yoonetsa Cikondi Cathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
  • Tikhala Monga mwa Dzina Lathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • ‘Talaŵani, Muone Kuti Yehova ni Wabwino’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 91

NYIMBO 91

Nchito Yoonetsa Cikondi Cathu

Yopulinta

(Salimo 127:1)

  1. 1. Tifuna kupemphela;

    Kuti ‘se tiyamikile.

    Inu Yehova pa cikondi,

    Mwationetsa!

    Imwe mwatidalitsa,

    Pogwila nchito mwakhama.

    Takumangilani nyumbayi,

    Na manja athu.

    (KOLASI)

    Unali mwayi wapadela

    Kukumangilani nyumba.

    Tidzakutamandani M’lungu nthawi zonse

    Na kukutumikilani.

  2. 2. Ndife osangalala,

    Kuti tapeza mabwenzi!

    Tidzakumbukila nthawizi

    Ku umuyaya!

    Taona mzimu wanu,

    Pogwila nchito pamodzi.

    Dzina lanu talichukitsa;

    Kwa anthu onse!

    (KOLASI)

    Unali mwayi wapadela

    Kukumangilani nyumba.

    Tidzakutamandani M’lungu nthawi zonse

    Na kukutumikilani.

(Onaninso Sal. 116:1; 147:1; Aroma 15:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani