LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 58
  • Pemphero Langa Losonyeza Kudzipereka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphero Langa Losonyeza Kudzipereka
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pemphelo Langa Lodzipelekela kwa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova mwa Kuimba Nyimbo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 58

Nyimbo 58

Pemphero Langa Losonyeza Kudzipereka

(Mateyu 22:37)

1. Tengani mtima wanga

Cho’nadi uzikonda.

Maganizo tengani

Ndikutumikireni.

2. Manja anga tengani

Akutumikireni.

Tengani mawu anga,

Ndi’mbire Mfumu yanga.

3. Moyo wanga mu’tenge,

Zabwino ndizichite.

Yehova nditengeni,

Ndikusangalatseni.

(Onaninso Sal. 40:8; Yoh. 8:29; 2 Akor. 10:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani