LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mb phunzilo 6
  • Phunzilo 6

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzilo 6
  • Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Tinapangidwa Modabwitsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Phunzilo 5
    Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Phunzilo 1
    Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
mb phunzilo 6

Phunzilo 6

Salimo 139:14

Yang’ana zala zako zakumanja, ndipo nyang’anyitsa zala zako zakumiyendo.

Loza makutu ako ndi mphuno yako.

Ona miyendo imene imacititsa kuti uzithamanga, uzilumpha ndi kuti uzizungulila. Komanso kuti uzicita zinthu zosangalatsa!

Yang’ana pa kalilole, uonapo ciani?

Yehova anapanga zinthu zonse zokongola!

ZOCITA

Muŵelengeleni mwana wanu:

Salimo 139:14

Uzani mwana wanu kuti aloze:

Zala zakumanja Zala zakumiyendo Mphuno yake

Makutu ake Pakamwa pake

Pezani zinthu zobisika.

Nkhanu Cona (Pusi)

M’funseni mwana wanu:

Ndani analenga iwe ndi ine?

[Cithunzi 14]

[Cithunzi 15]

[Cithunzi 15]

[Cithunzi 16]

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani