LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsa. 5
  • Tinapangidwa Modabwitsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tinapangidwa Modabwitsa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Amakudziŵani
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Phunzilo 6
    Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • Nchito Zodabwitsa za Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kuyankha Mafunso A m’Baibulo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 September tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 135-141

Tinapangidwa Modabwitsa

Davide anali kuganizila za umboni woonetsa makhalidwe abwino a Mulungu amene amaonekela m’zinthu zimene anapanga. Iye anaseŵenzetsa moyo wake kutumikila Yehova mokhulupilika.

Mayi wa pakati ndi mwamuna wake m’nthawi zakale

Davide ataganizila kwambili za cilengedwe, anayamba kutamanda Yehova:

139:14

  • “Ndidzakutamandani cifukwa munandipanga modabwitsa”

139:15

  • “Mafupa anga sanali obisika kwa inu pamene munali kundipanga m’malo obisika, pamene munali kundiwomba ngati nsalu m’malo apansi kwambili padziko lapansi”

139:16

  • “Maso anu anandiona pamene ndinali mluza, ndipo ziwalo zanga zonse zinalembedwa m’buku lanu”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani