LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 5
  • Nchito Zodabwitsa za Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Nchito Zodabwitsa za Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Tinapangidwa Modabwitsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Mwa Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mulungu Amakudziŵani Bwino?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2018
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 5

NYIMBO 5

Nchito Zodabwitsa za Mulungu

Yopulinta

(Salimo 139)

  1. 1. Inu Mulungu mumadziŵa,

    Nikagona olo nikauka.

    Zilizonse ine nimaganiza,

    Inu Atate Yehova,

    muzidziŵa.

    Munaona ziwalo zanga,

    Pamene ninali kupangiwa.

    Palibe cimene cinabisika.

    Nidzakutamandani.

    ndinu wamphamvu.

    Nzelu zanu Mulungu n’zodabwitsa

    Zimenezi nimadziŵa bwino.

    Nikavutika mumanithandiza,

    Mzimu wanu umanilimbitsa.

    Yehova ningayende kuti

    Kumene ningakubisameni?

    M’manda kodi,

    kumwamba olo m’nyanja?

    Kulikonse imwe M’lungu munipeza.

(Onaninso Sal. 66: 3; 94: 19; Yer. 17:10.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani