LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 110
  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Nchito Zodabwitsa za Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tinapangidwa Modabwitsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Kodi Shelo ndi Hade N’ciani?
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
  • Mwa Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 110

Nyimbo 110

Ntchito Zodabwitsa za Mulungu

(Salimo 139)

1. Inu Mulungu mumadziwa

Ndikagona ndipo ndikadzuka.

Mumadziwanso maganizo anga

Ngakhale mawu anga

Ndi njira zanga.

Munaona malo ’bisika.

Panthawi yomwe ndinali m’mimba.

Ziwalo zangatu zinalembedwa,

Ndikutamandani ndinu wodabwitsa.

Nzeru zanu Mulungu n’zodabwitsa.

Zimenezi ndithu ndikudziwa.

Ndikaopa kuphimbidwa ndi mdima

Mzimu wanu M’lungu undipeza.

N’kuti komwe ndingabisale

Komwe inu simungandione?

Kumwamba kodi kapena kumanda,

Mumdima, m’nyanja?

Ayi ndithu kulibe.

(Onaninso Sal. 66:3; 94:19; Yer. 17:10.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani