Tsiku Lacitatu
“Limba mtima ndipo ucite zinthu mwamphamvu. Yembekezela Yehova” —SALIMO 27:14
KUM’MAŴA
- 8:20 Vidiyo ya Nyimbo 
- 8:30 Nyimbo Na. 73 na Pemphelo 
- 8:40 YOSIILANA: Zocitika Zam’tsogolo Zimene Zidzafuna Kulimba Mtima - Kulengeza “Bata ndi Mtendele!” (1 Atesalonika 5:2, 3) 
- Kuwonongedwa kwa Babulo Wamkulu (Chivumbulutso 17:16, 17) 
- Kulengeza Uthenga wa Matalala (Chivumbulutso 16:21) 
- Kuukila kwa Gogi wa Magogi (Ezekieli 38:10-12, 14-16) 
- Aramagedo (Chivumbulutso 16:14, 16) 
- Nchito Yaikulu Yokonzanso Zinthu (Yesaya 65:21) 
- Ciyeso Cotsiliza (Chivumbulutso 20:3, 7, 8) 
 
- 10:10 Nyimbo Na. 8 na Zilengezo 
- 10:20 NKHANI YA ANTHU ONSE: Kodi Ciyembekezo ca Ciukililo Cimatithandiza Bwanji Kukhala Olimba Mtima? (Maliko 5:35-42; Luka 12:4, 5; Yohane 5:28, 29; 11:11-14) 
- 10:50 Cidule ca Nsanja ya Mlonda 
- 11:20 Nyimbo Na. 151 na Kupumula 
KUMASANA
- 12:35 Vidiyo ya Nyimbo 
- 12:45 Nyimbo Na. 5 
- 12:50 FILIMU YAIKULU: Nkhani ya Yona—Kutengapo Phunzilo pa Kulimba Mtima na Cifundo (Yona 1-4) 
- 13:40 Nyimbo Na. 71 na Zilengezo 
- 13:50 Ali ku Mbali Yathu ni Ambili Kuposa Adani Athu! (Deuteronomo 7:17, 21; 28:2; 2 Mafumu 6:16; 2 Mbiri 14:9-11; 32:7, 8, 21; Yesaya 41:10-13) 
- 14:50 Nyimbo na Pemphelo Lothela