LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/15 tsa. 4
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • Galamukani! January
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 12/15 tsa. 4

Maulaliki Acitsanzo

Nsanja ya Mlonda November-December

“Kodi munadzifunsapo kuti n’cifukwa ciani timachedwa Mboni za Yehova? [Yembekezani yankho.] Yankho lake tingalipeze m’Baibulo mmene Mulungu amatiuza dzina lake. [Ŵelengani Salimo 83:18.] Monga Mboni za Yehova, timalengeza uthenga wabwino wokhudza Yehova ndi colinga cake kwa anthu. Magazini iyi iyankha mafunso amene anthu amakhala nao okhudza Mboni za Yehova.”

Galamukani! January

“Ndakubweletselani magazini iyi ya Galamukani! ya mwezi uno. [Patsani munthuyo magazini.] Onani funso limene lili pa tsamba 2 komanso mayankho amene alipo. Kodi inu muona bwanji? [Yembekezani yankho.] Magazini iyi itithandiza kuona mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kuona zinthu moyenelela pamoyo wathu.”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani