LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsa. 6
  • “Yehova Ndi Wamkulu ndi Woyenela Kutamandidwa Kwambili”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Yehova Ndi Wamkulu ndi Woyenela Kutamandidwa Kwambili”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Yehova Amathandiza Odwala
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 September tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 142-150

“Yehova Ndi Wamkulu ndi Woyenela Kutamandidwa Kwambili”

145:1-5

Nyenyezi kumwamba

Pamene anaona kuti ukulu wa Yehova ni wosasanthulika, Davide analimbikitsidwa kumutamanda kwamuyaya

145:10-12

Mofanana ndi Davide, atumiki okhulupilika a Yehova amakamba za nchito zake zamphamvu tsiku lililonse

Banja la m’nthawi yakale liyang’ana nyenyezi kumwamba

145:14

Munthu wagwila dzanja la mnzake kuti amuthandize

Davide sanakaikile kuti Yehova amafuna kusamalila atumiki ake onse ndi kuti ali ndi mphamvu zocita zimenezo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani