LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 November tsa. 4
  • Tizitengelapo Phunzilo pa Zolakwa Zathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tizitengelapo Phunzilo pa Zolakwa Zathu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Zimene Tiphunzilamo m’Buku la Yona
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yehova Anamulezela Mtima Yona
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yona Ndi Cinsomba
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Yona
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 November tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | OBADIYA 1–YONA 4

Tizitengelapo Phunzilo pa Zolakwa Zathu

Nkhani ya Yona imaonetsa kuti Yehova saleka kutithandiza tikalakwitsa. Ndiponso, amayembekezela kuti titengelepo phunzilo pa zolakwa zathu, na kupanga masinthidwe ofunikila.

Yona 1:3

Kodi Yona analakwitsa ciani atapatsidwa nchito na Yehova?

Mseu wa pa nyanja kucoka ku Yopa kupita ku Tarisi

Yona 2:1-10

Kodi Yona anapempha ciani kwa Yehova? Nanga Yehova anamuyankha bwanji?

Yona apemphela m’mbali mwa nyanja

Yona 3:1-3

Kodi Yona anaonetsa bwanji kuti anatengelapo phunzilo pa zolakwa zake?

Mseu wa pa nyanja kucoka ku Yopa kupita ku Tarisi
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani