LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 November tsa. 8
  • Zimene Tiphunzilamo m’Buku la Yona

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Tiphunzilamo m’Buku la Yona
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Tizitengelapo Phunzilo pa Zolakwa Zathu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yehova Anamulezela Mtima Yona
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yona Ndi Cinsomba
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Yona
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 November tsa. 8

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Zimene Tiphunzilamo m’Buku la Yona

Yehova anasunga nkhani za amuna na akazi okhulupilika m’Mau ake, n’colinga cakuti titengepo maphunzilo ofunikila. (Aroma 15:4) Kodi munaphunzila ciani m’buku la Yona? Tambani vidiyo yakuti Kulambila kwa Pabanja: Yona Anaphunizilapo Kanthu pa Cifundo ca Yehova. Ndiyeno yankhani mafunso aya:

  • Ni mavuto ati amene ofalitsa atatu mu vidiyoyi anakumana nawo?

  • Kodi buku la Yona lingatilimbikitse bwanji tikapatsidwa uphungu kapena kutaikidwa mwayi wa utumiki?— (1 Sam. 16:7; Yona 3:1, 2.)

  • Kodi nkhani ya Yona ingatithandize bwanji kukhala na maganizo abwino a gawo lathu?— (Yona 4:11; Mat. 5:7.)

  • Ngati tidwala matenda osathelapo, kodi zimene zinacitikila Yona zingatitonthoze bwanji?— (Yona 2:1, 2, 7, 9.)

  • Mwaphunzila ciani mu vidiyoyi za kufunika koŵelenga Baibo na kusinkha-sinkha?

M’bale ni wokhumudwa cifukwa cotaikilidwa utumiki; mlongo akuganiza kuti mwininyumba sangamvetsele; mlongo walandila uthenga wacisoni kucokela kwa dokota
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani