LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 December tsa. 6
  • Tengelani Citsanzo ca Mtumwi Paulo Polalikila na Kuphunzitsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tengelani Citsanzo ca Mtumwi Paulo Polalikila na Kuphunzitsa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Tengelani Kudzicepetsa kwa Mariya
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Kodi Mumawaona Bwanji Anthu a mu Gawo Lanu?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Muzionetsa Kuyamikila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Amuna Odzicepetsa Amaphunzitsa Ena Nchito na Kuwagaŵila Maudindo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 December tsa. 6
Paulo akulalikila pa msika

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 17-18

Tengelani Citsanzo ca Mtumwi Paulo Polalikila na Kuphunzitsa

17:2, 3, 17, 22, 23

Tingatengele bwanji citsanzo ca mtumwi Paulo?

  • Kulalikila pa msika

    Tiziseŵenzetsa Malemba pokambilana na anthu, komanso kuwafotokoza mogwilizana na omvela athu

  • Kulalikila mu msewu

    Tizilalikila kumene kumapezeka anthu, komanso pa nthawi yoyenela

  • M’bale akuseŵenzetsa Baibo ya munthu amene akumulalikila

    Mosamala tizipewa kutsutsa zimene ena amakhulupilila n’colinga cakuti tiyale maziko abwino a ulaliki

ZOFUNIKA KUSINKHA-SINKHA: M’gawo la mpingo wathu, n’kuti kumene ningapeze anthu ambili owalalikila? Nanga ni pa nthawi iti?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani