LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsa. 6
  • Amuna Odzicepetsa Amaphunzitsa Ena Nchito na Kuwagaŵila Maudindo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Amuna Odzicepetsa Amaphunzitsa Ena Nchito na Kuwagaŵila Maudindo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Zimenezo Uziphunzitse kwa Amuna Okhulupilika’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • N’cifukwa Ciani Kudzicepetsa N’kofunikabe?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Mukhoza Kukhalabe Wodzicepetsa Ngakhale pa Ciyeso
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Tengelani Citsanzo ca Mtumwi Paulo Polalikila na Kuphunzitsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 August tsa. 6
Zithunzi: Mkulu amene ni ciyamba kale akuphunzitsa m’bale mwakhama kuti ayenelele maudindo aakulu mu mpingo. 1. M’bale wagwilila maikolofoni pamene mkulu amene ni ciyamba kale apeleka ndemanga pamsonkhano. 2. M’bale wapelekeza mkulu amene ni ciyamba kale ku ulendo waubusa. 3. M’bale, tsopano mkulu, akukamba pa miting’i ya akulu. 4. Mkulu watsopano acititsa ‘Nsanja ya Mlonda.’ Mkulu amene ni ciyamba kale akuwelenga mapalagilafu.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 17–18

Amuna Odzicepetsa Amaphunzitsa Ena Nchito na Kuwagaŵila Maudindo

18:17, 18, 21, 22, 24, 25

Abale amene ni aciyamba kale, angaonetse kudzicepetsa, cikondi, komanso kuzindikila, pamene aphunzitsa nchito anyamata na kuwagawila maudindo. Motani?

  • Sankhani abale amene angathe kusenza maudindo owonjezeleka m’gulu la Yehova

  • Afotokozeleni momveka bwino zimene ayenela kucita kuti aigwile bwino nchitoyo

  • Apatseni ndalama, zida, komanso thandizo limene angafunike kuti agwile nchitoyo

  • Muziona mmene m’baleyo akugwilila nchito, na kumuuza kuti muli na cidalilo coti adzaigwila bwino nchitoyo

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ni maudindo ena ati amene ningapatseko ena?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani