LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 December tsa. 5
  • Nkhondo ya Mulungu Idzathetsa Nkhondo Zonse

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Nkhondo ya Mulungu Idzathetsa Nkhondo Zonse
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Kondani Cilungamo, Danani Nako Kusamvela Malamulo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Mapeto A Zoipa Zonse
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 December tsa. 5
Lupanga lalitali likutuluka pakamwa pa Yesu, ndipo gulu lake lankhondo la kumwamba lakwela pa mahosi oyela

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | CHIVUMBULUTSO 17-19

Nkhondo ya Mulungu Idzathetsa Nkhondo Zonse

19:11, 14-16, 19-21

N’cifukwa ciani Yehova, “Mulungu wacikondi ndi wamtendele” anapatsa Mwana wake amene ni “Kalonga Wamtendele” nchito yomenya nkhondo?​—2 Akor. 13:11; Yes. 9:6.

  • Yehova na Yesu amakonda cilungamo ndipo amadana na zoipa

  • Mtendele weni-weni na cilungamo zidzakhalapo kokha ngati anthu oipa acotsedwapo

  • Gulu lankhondo lakumwamba la Mulungu limene ‘likumenya nkhondo mwacilungamo,’ laimilidwa na mahosi oyela, litavala zovala zapamwamba, zoyela bwino, za mbee!

Tingacite ciani kuti tikapulumuke pa nkhondo yapadela imeneyi?​—Zef. 2:3

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani