LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 March tsa. 8
  • Samalani na Kunyada Komanso Kudzidalila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Samalani na Kunyada Komanso Kudzidalila
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Nkhani Zofanana
  • “Ine Ndine . . . Colowa Cako”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Mmene Yehova Amatsogolela Anthu Ake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Pitilizani Kupempha Citsogozo ca Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Anapandukila Yehova
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 March tsa. 8
Kora pamodzi na gulu la amuna aciisiraeli akukangana na Mose na Aroni.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Samalani na Kunyada Komanso Kudzidalila

Kora anapandukila makonzedwe a Yehova cifukwa anali wonyada komanso wodzidalila (Num. 16:1-3; w11 9/15 27 ¶12)

Kora anali Mlevi wolemekezeka ndipo anali na mautumiki ambili apadela (Num. 16:8-10; w11 9/15 27 ¶11)

Maganizo olakwika a Kora anabweletsa mavuto aakulu (Num. 16:32, 35)

Tisalole zinthu zimene tacita mu utumiki wa Yehova kutipangitsa kukhala wonyada na wodzidalila. Ngati takhala zaka zambili m’coonadi kapena ngati tili na maudindo aakulu, m’pamenenso tifunika kukhala odzicepetsa kwambili.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani