LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 September tsa. 9
  • Zimene Tingaphunzile pa Nkhani ya Agibeoni

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Tingaphunzile pa Nkhani ya Agibeoni
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Nkhani Zofanana
  • Agibeoni Anzelu
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Yoswa na Agibeoni
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yehova Anawamenyela Nkhondo Aisiraeli
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Malangizo Othela a Yoswa kwa Aisiraeli
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 September tsa. 9
Zithunzi: Nchito zosiyanasiyana zimene Agibeoni anali kugwila. 1. Mwamuna wanyamula mtolo waukulu wa nkhuni. 2. Mwamuna akumanga mtolo wa nkhuni. 3. Mwamuna wanyamula madzi poseŵenzetsa joko.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zimene Tingaphunzile pa Nkhani ya Agibeoni

Agibeoni anacita zinthu mwanzelu (Yos. 9:3-6; it-1 930-931)

Akulu a Isiraeli sanacite zinthu mwanzelu cifukwa sanafunsile kwa Yehova (Yos. 9:14, 15; w11 11/15 8 ¶14)

Agibeoni anatumikila Aisiraeli modzicepetsa (Yos. 9:25-27; w04 10/15 18 ¶14)

Agibeoni anali kugwila nchito zotsika cifukwa anafuna kuti Yehova awayanje. Kodi tingatengele bwanji citsanzo cawo ca kudzicepetsa masiku ano?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani