LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 March tsa. 4
  • “Yehova Ndiye Mwini Nkhondo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Yehova Ndiye Mwini Nkhondo”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • “Yehova Ndiye Mwini Nkhondo”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2016
  • Kodi Mukumbukila?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Khalanibe Odzicepetsa Zinthu Zikakuyendelani Bwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Davide Sanacite Mantha
    Phunzitsani Ana Anu
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 March tsa. 4
Goliyati, amene ni wamtali kwambili kuposa womunyamulila cishango, akunyoza Davide m’bwalo lomenyela nkhondo.

Davide wayang’anizana na Goliyati

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Yehova Ndiye Mwini Nkhondo”

Cikhulupililo ca Davide mwa Yehova cinali cozikidwa pa zimene anaphunzila na zimene zinamucitikila pa umoyo (1 Sam. 17:36, 37; wp16.5 11 ¶2-3)

Davide sanadziyelekezele na Goliyati, koma anayelekezela Goliyati na Yehova (1 Sam. 17:45-47; wp16.5 11-12)

Yehova anathandiza Davide kugonjetsa mdani wamphamvu komanso woopsa (1 Sam. 17:48-50; wp16.5 12 ¶4; onani cithunzi ca pacikuto)

Munthu akutayila m’bini paketi ya ndudu.

Nthawi zina, tingakhale na zopinga zazikulu monga cizunzo kapena cizoloŵezi coipa. Ngati tiona kuti mavuto athu ni aakulu kwambili, tizikumbukila kuti ni aang’ono tikawayelekezela na mphamvu zopanda malile za Yehova.—Yobu 42:1, 2.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani