LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsa. 16
  • Seŵenzetsani Nkhani Zongocitika Kumene mu Ulaliki

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Seŵenzetsani Nkhani Zongocitika Kumene mu Ulaliki
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Khalani Okonzeka Kusintha Ulaliki
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Kuphunzitsa Coonadi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Kuseŵenzetsa Mwaluso Zida Zophunzitsila za mu Thuboksi Yathu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Mawu Oyamba
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 May tsa. 16
Mlongo akukonzekela ulaliki. Ali na kathilakiti m’manja, ndipo akufufuza nyuzi pa kompyuta yake.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Seŵenzetsani Nkhani Zongocitika Kumene mu Ulaliki

Pa utumiki wake, Yesu anaseŵenzetsa nkhani zongocitika kumene pophunzitsa anthu. (Luka 13:1-5) Inunso mungaseŵenzetse nkhani zongocitika kumene pothandiza anthu kucita cidwi na uthenga wa Ufumu. Pambuyo pofotokoza za kukwela mtengo kwa zinthu, tsoka la zacilengedwe, zacipolowe, kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza bongo, kapena nkhani zina zotelo, funsani funso lopangitsa munthu kuganiza. Mungafunse kuti: “Kodi muganiza kuti mavuto monga . . . adzatha?” kapena “Kodi muona kuti n’ciyani cingathetse vuto la . . . ?” Kenako muŵelengeleni vesi ya m’Baibo yogwilizana na nkhaniyo. Ngati munthuyo waonetsa cidwi, muonetseni vidiyo kapena mugaŵileni cofalitsa ca mu Thuboksi yathu. Pamene tikuyesetsa kuwafika pamtima anthu m’gawo lathu, ‘tizicita zinthu zonse cifukwa ca uthenga wabwino.’—1 Akor. 9:22, 23.

Ni nkhani ziti zimene zingakope cidwi ca anthu m’gawo lanu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani