LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 July tsa. 11
  • Anagwila Nchito Molimbika Cifukwa Cokonda Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Anagwila Nchito Molimbika Cifukwa Cokonda Yehova
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Phindu la Nzelu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Solomo Amanga Kacisi
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Pemphelo la Solomo Lodzicepetsa Komanso Locokela Pansi pa Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Kacisi wa Yehova
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 July tsa. 11
Mfumu Solomo ali pa malo omangapo kacisi, ndipo akumvetsela mwachelu pamene wanchito akumufotokozela mapulani a kamangidwe ka kacisiyo.

Mfumu Solomo akuona mmene nchito yomanga kacisi ikuyendela

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Anagwila Nchito Molimbika Cifukwa Cokonda Yehova

Solomo anagwilitsa nchito zipangizo zabwino kwambili pomanga kacisi (1 Maf. 5:6, 17; w11 2/1 15)

Anthu ambili anagwilako nchitoyo (1 Maf. 5:13-16; it-1 424; it-2 1077 ¶1)

Solomo na anthuwo anagwila nchito molimbika kwa zaka 7 kuti amalize kumanga kacisi (1 Maf. 6:38; onani cithunzi ca pacikuto)

Cifukwa cokonda Yehova, Solomo na anthuwo anamanga kacisi wokongola amene anapangitsa kuti Yehova atamandike. Koma cacisoni n’cakuti, mibadwo ya m’tsogolo mwawo inalibe cangu pa kulambila koona. Iwo analeka kusamalila kacisiyo, ndipo pambuyo pake kacisiyo anawonongedwa.

Abale na alongo akuyeletsa Nyumba ya Ufumu mosangalala. Kumbuyo kwawo, ena akuponya zopeleka m’bokosi la zopeleka, akukambilana, na kusonkhanitsa zofalitsa kuti abale na alongo atengepo pambuyo pake.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nikucita ciyani kuti nikhalebe wokangalika polambila Yehova?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani